News from Mangochi
Stay current with all the latest and breaking news about Mangochi, compare headlines and perspectives between news sources on stories happening today. In total, 8 stories have been published about Mangochi which Ground News has aggregated in the past 3 months.
Suggest a source
Looking for a source we don't already have? Suggest one here.Top Mangochi News
Latest News Stories
Peter Mutharika · MangochiFikitsani uthengawu ku Mangochi kwa a Mutharika: zobwelera m’boma ndi maloto chabe, a Malawi onse maso nga! pa Chakwera, watero ndi nduna ya Maboma Aang’ono a Richard Chimwendo Banda. Polankhula potsekera zokambirana mu nyumba ya malamulo lero, a Chimwendo Banda ati chipani chotsutsa cha DPP chinatuluka m’boma ndipo sichibweleranso. Iwo ati a Malawi ambiri akukumbukirabe […] The post DPP sidzabweleranso m’boma ndipo 2025 Chakwera awina ndi 70% –…See the Story
DPP sidzabweleranso m'boma ndipo 2025 Chakwera awina ndi 70% - Chimwendo Malawi 24 | Latest News from Malawi
Mangochi · MangochiIn Mangochi, a suspected criminal known identified as Allen M’bwana has been shot to death by police after he wounded a police officer while resisting arrest in the wee early hours of Sunday at Makawa. According to police records, M’bwana, an ex-convict was also a well-known habitual criminal and had been wanted by police in […] The post Man shot dead after injuring police officer appeared first on Malawi 24.See the Story
Man shot dead after injuring police officer Malawi 24 | Latest News from Malawi
Mangochi · MangochiBwalo la milandu la Senior Resident Magistrate m’boma la Mangochi, lagamula anthu awiri omwe amabera anthu ndalama pomanama kuti mankhwala omwe amagulitsa amachiza matenda a AIDS kuti alipile chindapusa cha ndalama zokwana K2,450,000 aliyese. Posachedwapa, apolisi m’boma la Mangochi anamanga mayi Mary Saidi a zaka 25 komaso a Molly Kainga powaganizira kuti akhala akubera anthu […] The post Obera anthu ponama kuti mankhwala awo amachiza AIDS agam…See the Story
Obera anthu ponama kuti mankhwala awo amachiza AIDS agamulidwa chindapusa cha K4.9 miliyoni Malawi 24 | Latest News from Malawi
Mangochi · MangochiMalawi Police in the lakeshore district of Mangochi are keeping in custody Mary Julius, 25,on allegations that she was selling gentamicin injection as an HIV/AIDS cure. Julius was arrested over the weekend at Abuja Bus Depot within the township.See the Story